Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan YOHANE 5

1

YOHANE 5:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Indetu, indetu, ndinena kwa inu, kuti iye wakumva mau anga, ndi kukhulupirira Iye amene anandituma Ine, ali nao moyo wosatha, ndipo salowa m'kuweruza, koma wachokera kuimfa, nalowa m'moyo.

Konpare

Eksplore YOHANE 5:24

2

YOHANE 5:6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu, pakuona ameneyo alikugona, ndipo anadziwa kuti anatero nthawi yaikulu pamenepo, ananena naye, Ufuna kuchiritsidwa kodi?

Konpare

Eksplore YOHANE 5:6

3

YOHANE 5:39-40

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Musanthula m'malembo, popeza muyesa kuti momwemo muli nao moyo wosatha; ndipo akundichitira Ine umboni ndi iwo omwewo; ndipo simufuna kudza kwa Ine, kuti mukhale nao moyo.

Konpare

Eksplore YOHANE 5:39-40

4

YOHANE 5:8-9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu ananena naye, Tauka, yalula mphasa yako, nuyende. Ndipo pomwepo munthuyu anachira, nayalula mphasa yake, nayenda. Koma tsiku lomwelo linali la Sabata.

Konpare

Eksplore YOHANE 5:8-9

5

YOHANE 5:19

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pamenepo Yesu anayankha nati kwa iwo, Indetu, indetu ndinena kwa inu, sakhoza Mwana kuchita kanthu pa yekha, koma chimene aona Atate achichita, ndicho. Pakuti zimene Iye azichita, zomwezo Mwananso azichita momwemo.

Konpare

Eksplore YOHANE 5:19

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak YOHANE 5

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo