Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan YOHANE 17

1

YOHANE 17:17

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Patulani iwo m'choonadi; mau anu ndi choonadi.

Konpare

Eksplore YOHANE 17:17

2

YOHANE 17:3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma moyo wosatha ndi uwu, kuti akadziwe Inu Mulungu woona yekha, ndi Yesu Khristu amene munamtuma.

Konpare

Eksplore YOHANE 17:3

3

YOHANE 17:20-21

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma sindipempherera iwo okha, komanso iwo akukhulupirira Ine chifukwa cha mau ao; kuti onse akakhale amodzi, monga Inu Atate mwa Ine, ndi Ine mwa Inu, kuti iwonso akakhale mwa Ife: kuti dziko lapansi likakhulupirire kuti Inu munandituma Ine.

Konpare

Eksplore YOHANE 17:20-21

4

YOHANE 17:15

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Sindipempha kuti muwachotse iwo m'dziko lapansi, koma kuti muwasunge iwo kuletsa woipayo.

Konpare

Eksplore YOHANE 17:15

5

YOHANE 17:22-23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo ulemerero umene mwandipatsa Ine ndapatsa iwo; kuti akhale amodzi, monga Ife tili mmodzi; Ine mwa iwo, ndi Inu mwa Ine, kuti akhale angwiro mwa mmodzi; kuti dziko lapansi lizindikire kuti Inu munandituma Ine, nimunawakonda iwo, monga momwe munakonda Ine.

Konpare

Eksplore YOHANE 17:22-23

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak YOHANE 17

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo