Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan GENESIS 7

1

GENESIS 7:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.

Konpare

Eksplore GENESIS 7:1

2

GENESIS 7:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Konpare

Eksplore GENESIS 7:24

3

GENESIS 7:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.

Konpare

Eksplore GENESIS 7:11

4

GENESIS 7:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali pa dziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa pa dziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.

Konpare

Eksplore GENESIS 7:23

5

GENESIS 7:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo mvula inali pa dziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.

Konpare

Eksplore GENESIS 7:12

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo