Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan GENESIS 19

1

GENESIS 19:26

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma mkazi wake anacheuka ali pambuyo pake pa Loti, nasanduka mwala wamchere.

Konpare

Eksplore GENESIS 19:26

2

GENESIS 19:16

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma anachedwa; ndipo anthuwo anamgwira dzanja lake, ndi dzanja la mkazi wake ndi dzanja la ana ake akazi awiri; chifukwa cha kumchitira chifundo Yehova; ndipo anamtulutsa iye, namuika kunja kwa mudzi.

Konpare

Eksplore GENESIS 19:16

3

GENESIS 19:17

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo panali pamene anawatulutsa iwo kunja, anati, Tapulumuka ndi moyo wako; usacheuke, usakhale pachigwa paliponse; thawira kuphiri, kuti unganyeke.

Konpare

Eksplore GENESIS 19:17

4

GENESIS 19:29

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo panali pamene Mulungu anaononga midzi ya m'chigwa, Mulungu anakumbukira Abrahamu, natulutsa Loti pakati pa chionongeko, pamene anaononga midzi m'mene anakhalamo Loti.

Konpare

Eksplore GENESIS 19:29

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo