Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan MACHITIDWE A ATUMWI 9

1

MACHITIDWE A ATUMWI 9:15

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma Ambuye anati kwa iye, Pita; pakuti iye ndiye chotengera changa chosankhika, chakunyamula dzina langa pamaso pa amitundu ndi mafumu ndi ana a Israele

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 9:15

2

MACHITIDWE A ATUMWI 9:4-5

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo anagwa pansi, namva mau akunena naye, Saulo, Saulo, Undilondalonderanji? Koma anati, Ndinu yani Mbuye? Ndipo anati, Ndine Yesu amene umlondalonda

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 9:4-5

3

MACHITIDWE A ATUMWI 9:17-18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anachoka Ananiya, nalowa m'nyumbayo; ndipo anaika manja ake pa iye, nati, Saulo, mbale, Ambuye wandituma ine, ndiye Yesu amene anakuonekerani pa njira wadzerayo, kuti upenyenso, ndi kudzazidwa ndi Mzimu Woyera. Ndipo pomwepo padagwa kuchoka m'maso mwake ngati mamba, ndipo anapenyanso; ndipo ananyamuka nabatizidwa

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 9:17-18

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak MACHITIDWE A ATUMWI 9

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo