YouVersion का प्रतीक चिन्ह
बाइबिलयोजनाएँवीडियो
ऐप प्राप्त करें
भाषा चयनकर्ता
खोज चिह्न

GENESIS 8से लोकप्रिय बाइबिल छंद

1

GENESIS 8:21-22

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anamva chonunkhira chakukondweretsa; nati Yehova m'mtima mwake, Sindidzatembereranso konse nthaka chifukwa cha munthu; pakuti ndingaliro ya mtima wa munthu ili yoipa kuyambira pa unyamata wake; sindidzaphanso konse zinthu zonse zamoyo, monga momwe ndachitiramo. Pakukhalabe masiku a dziko lapansi, nthawi yakubzala ndi yakukunkha, chisanu ndi mafundi, malimwe ndi msakasa, usana ndi usiku sizidzalekai.

तुलना

खोजें GENESIS 8:21-22

2

GENESIS 8:20

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Nowa anamanga guwa la nsembe la Yehova; natengapo nyama zodyedwa zonse ndi mbalame zodyedwa zonse napereka nsembe zopsereza paguwapo.

तुलना

खोजें GENESIS 8:20

3

GENESIS 8:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Mulungu anakumbukira Nowa ndi zamoyo zonse, ndi nyama zonse zimene zinali pamodzi naye m'chingalawamo; ndipo Mulungu anapititsa mphepo pa dziko lapansi, naphwa madzi

तुलना

खोजें GENESIS 8:1

4

GENESIS 8:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo njiwa inadza kwa iye madzulo; ndipo, taonani, m'kamwa mwake munali tsamba la azitona lothyoledwa: ndipo anadziwa Nowa kuti madzi analimkuphwa pa dziko lapansi.

तुलना

खोजें GENESIS 8:11

पिछला अध्याय
अगला अध्याय
YouVersion

हर दिन परमेश्वर के साथ घनिष्ठता तलाशने के लिए आपको प्रोत्साहित और चुनौती देना।

मिनिस्ट्री

के विषय में

पेशा

स्वयंसेवक

ब्लॉग

प्रेस

उपयोगी लिंक

सहायता

योगदान

बाईबिल की अन्य संस्करणे

ऑडियो बाइबिल

बाइबिल भाषाएँ

आज का पद्य


एक डिजिटल मिनिस्ट्री, ये वाले से -

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

निजी नीतिशर्तें
भेद्यता प्रकटीकरण कार्यक्रम
फेसबुकट्विट्टरइंस्टाग्रामयूट्यूबपिंटरेस्ट

होम

बाइबिल

योजनाएँ

वीडियो