לוגו של YouVersion
כתבי הקודשתכניותקטעי וידאו
הורד את האפליקציה
בורר שפה
סמל חיפוש

פסוקים פופולריים מ- Yoh. 2

1

Yoh. 2:11

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Yesu adaonetsa chizindikiro chake choyambachi m'mudzi wa Kana m'dera la Galileya. Pamenepo adaonetsa ulemerero wake, ndipo ophunzira ake adamkhulupirira.

השווה

חקרו Yoh. 2:11

2

Yoh. 2:4

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Yesu adayankha kuti, “Mai, kodi mukuti nditani? Nthaŵi yangatu siinafike.”

השווה

חקרו Yoh. 2:4

3

Yoh. 2:7-8

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Tsono Yesu adauza anyamata aja kuti, “Dzazani mbiyazi ndi madzi.” Ndipo adazidzaza mpaka m'milomo. Pambuyo pake adaŵauza kuti, “Tsopano tungani, kaperekeni kwa mkulu wa phwando,” Iwowo adakaperekadi.

השווה

חקרו Yoh. 2:7-8

4

Yoh. 2:19

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Yesu adaŵayankha kuti, “Gwetsani nyumba ya Mulungu ino, Ine ndidzaimanganso masiku atatu.”

השווה

חקרו Yoh. 2:19

5

Yoh. 2:15-16

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Apo Yesu adapanga mkwapulo wazingwe nayamba kuŵatulutsira onse kunja, pamodzi ndi nkhosa ndi ng'ombe zao zomwe. Adagubudula matebulo a osinthitsa ndalama aja, naŵamwazira ndalama zao. Ndipo adalamula ogulitsa nkhunda aja kuti, “Izi zitulutseni muno. Nyumba ya Atate anga musaisandutse nyumba yochitiramo malonda.”

השווה

חקרו Yoh. 2:15-16

לפרק הקודם
לפרק הבא
YouVersion

מעודד ומאתגר אתכם לקשר הדוק עם אלוהים בכל יום.

מִשׂרָד

אודות

קריירה

התנדב

בלוג

לחץ

קישורים שימושיים

עזרה

תרום

גרסאות הכתובים

אודיו הכתובים

שפות התנ"ך

הפסוק של היום


משרד דיגיטלי של

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

מדיניות פרטיותתנאים
תוכנית לגילוי חולשות אחראי
פייסבוקטוויטראינטגרםיוטיובפינטרסט

בית

כתבי הקודש

תכניות

קטעי וידאו