1
Maluko 4:39-40
Nyanja
NTNYBL2025
Ndiipo Yesu wadauka ni kuunyindila mwela, “Khala chete!” Pampajha mwela udasiya ni nyanja idagona. Chimwecho Yesu wadaakambila oyaluzidwa wake, “Ndande yanji muopa? Bwanji, mkali mlibe chikulupililo?”
Compare
Maluko 4:39-40 ખોજ કરો
2
Maluko 4:41
Oyaluzidwa wake adaopa kupunda, adafunjhana, “Mundhu wa mtundu wanji uyu mbaka mwela umvela?”
Maluko 4:41 ખોજ કરો
3
Maluko 4:38
Yesu wadali kumbuyo kwa lijha boti wadatogonela philo, oyaluzidwa wake adamuucha ni kumkambila, “Oyaluza, simganizila kuti ife titobila?”
Maluko 4:38 ખોજ કરો
4
Maluko 4:24
Chinchijha wadaakambila, “Mkhale maso ni yayo muyavela. Chimchijha umo mujhichocha kuvechela mawu nde chimwecho Mnungu siwakuchite ulijhiwe mawu kupunda.
Maluko 4:24 ખોજ કરો
5
Maluko 4:26-27
Yesu wadaendekela kukamba, “Ufumu wa Mnungu ulingati chimwechi. Mundhu mmojhi wadamijha mbewu mmunda. Usiku wamagona, ni usana wakhala maso, mbeu zimela ni kukula popande iye siwajhiwa icho chichitika.
Maluko 4:26-27 ખોજ કરો
6
Maluko 4:23
Mchate icho mkambidwa!”
Maluko 4:23 ખોજ કરો
હોમ
બાઇબલ
યોજનાઓ
વિડિઓઝ