1
Maluko 3:35
Nyanja
NTNYBL2025
Mundhu waliwonjhe uyo wachita yayo wayafuna Mnungu, mmeneyo nde mkulu wanga ni mlongowanga ni maye wanga.”
Compare
Maluko 3:35 ખોજ કરો
2
Maluko 3:28-29
“Zenedi nikukambilani, machimo yonjhe yayo achita wandhu, ni kukafula kwawo konjhe, Mnungu siwalekelele. Nambho mundhu waliyonjhe uyo wamkafula Mzimu Woyela, kukafula kwake sikulekeleledwa muyaya. Ndande wachita machimo ya muyaya.”
Maluko 3:28-29 ખોજ કરો
3
Maluko 3:24-25
Ufumu uliwonjhe ukapatukana ni kubulana, ufumu umenewo siukhoza kulimba. Ikakhala wandhu a nyumba imojhi apatukana achinawene magulumagulu yayo yachuchana, nyumba imeneyo siikhoza kulimba.
Maluko 3:24-25 ખોજ કરો
4
Maluko 3:11
Wandhu yawo adali ni viwanda, yapo adamwona Yesu, adajhitaya panjhi pachogolo pake ni kukweza mvekelo, niakamba, “Iwe ni Mwana wa Mnungu!”
Maluko 3:11 ખોજ કરો
હોમ
બાઇબલ
યોજનાઓ
વિડિઓઝ