1
Matayo 26:41
Nyanja
NTNYBL2025
Chezelani ni kupembhela kuti msadalowa mu mayeselo. Mtima ufuna kuchita yayo yafunika, nambho thupi lilibe mbhavu.”
Compare
Matayo 26:41 ખોજ કરો
2
Matayo 26:38
Kumeneko wadaakambila, “Nili ni chisoni chachikulu mumtima mwanga icho chikhoza kunipha. Khalani pano ni muchezele pamojhi ni ine.”
Matayo 26:38 ખોજ કરો
3
Matayo 26:39
Wadapita pachogolo pang'ono, wadagwa panjhi chifufumimba ni kupembhela, “Atate wanga, ngati ikhozeka, nichocheleni chikho ichi cha mavuto! Chipano osati ngati umo nifunila ine, nambho ngati umo mufunila imwe.”
Matayo 26:39 ખોજ કરો
4
Matayo 26:28
uwu nde mwazi wanga uwo uchimikiza chipangano, umwazika ndande ya ambili dala machimo yao yalekeleledwe.
Matayo 26:28 ખોજ કરો
5
Matayo 26:26
Yapo amadya Yesu wadatenga bumunda, wadayamika, wadaubandhula, ni kwapacha oyaluzidwa wake nikukamba, “Tengani mudye, ili nithupi langa.”
Matayo 26:26 ખોજ કરો
6
Matayo 26:27
Ndiipo wadatenga chikho, wadayamika Mnungu, ni kwaapacha oyaluzidwa wake niwakamba, “Mwaonjhe mchimwele chikho ichi
Matayo 26:27 ખોજ કરો
7
Matayo 26:40
Ndiipo wadabwela kwa oyaluzidwa wake ni kwaapheza agona, wadamkambila Petulo, “Ikhala bwanji simdakhoze kuchezelela ni ine ata kwa saa imojhipe?
Matayo 26:40 ખોજ કરો
8
Matayo 26:29
Nikukambilani, sinimwanjho divai iyi mbaka siku ilo sinimwe divai yachipano ni anyiimwe mu Ufumu wa Atate wanga.”
Matayo 26:29 ખોજ કરો
9
Matayo 26:75
Ndiipo Petulo wadakumbukila mau yajha wadakamba Yesu, “Tambala wakali osalile, siunikane katatu.” Wadapita kubwalo, wadalila kwa kubuula.
Matayo 26:75 ખોજ કરો
10
Matayo 26:46
Imani tijhipita. Yujha waning'anamuka watokujha.”
Matayo 26:46 ખોજ કરો
11
Matayo 26:52
Ndiipo Yesu wadamkambila, “Bwezela upanga wako mmalo mwake, pakuti waliyonjhe wakupha kwa upanga, siwaphedwe kwa upanga.
Matayo 26:52 ખોજ કરો
હોમ
બાઇબલ
યોજનાઓ
વિડિઓઝ