1
Matayo 25:40
Nyanja
NTNYBL2025
Mfumu siwaayanghe, ‘Zene nikukambilani, umo mwamchitila mmojhi wa anyiyawa abale wanga yawo sajhikoza, mwanichitila ine!’”
Compare
Matayo 25:40 ખોજ કરો
2
Matayo 25:21
Mkulu wake wadamkambila, ‘Wachita bwino, iwe ni mbowa wabwino ni ukhulupilika. Pakuti udakhulupilika kwa vindhu vochepa, chipano sinikupache vindhu va vikulu, majha ukondwele pamojhi ni mkulu wako!’
Matayo 25:21 ખોજ કરો
3
Matayo 25:29
Pakuti kila uyo wachitila njhito icho nampacha sinimchuluchile vina nayo siwakhale navo vambili. Nambho mundhu waliyonjhe uyo siwachitila njhito icho nimpacha, ata chaching'ono walinacho siwalandidwe.
Matayo 25:29 ખોજ કરો
4
Matayo 25:13
Ndiipo Yesu wadamalizila kukamba, “Mjhipenyelele pakuti simujhiwa siku kapina saa.”
Matayo 25:13 ખોજ કરો
5
Matayo 25:35
Nidali ni njala mdanipacha chakudya, ni nidali nilujho mdanipacha majhi ya kumwa, ni nidali mlendo mdanilandila mnyumba zanu.
Matayo 25:35 ખોજ કરો
6
Matayo 25:23
Mkulu wake wadakamba, ‘Wachita bwino, iwe ni mbowa wabwino ni okhulupilika. Pakuti udali wokhulupilika kwa vindhu vochepa, sinikuike uimilile vindhu va vikulu, majha ukondwele pamojhi ni mkulu wako!’
Matayo 25:23 ખોજ કરો
7
Matayo 25:36
Nidalibe njhalu mdaniveka, nidali odwala mdanidwaza ni nidali mndende mdaniyendela.’
Matayo 25:36 ખોજ કરો
હોમ
બાઇબલ
યોજનાઓ
વિડિઓઝ