YouVersion-logo
BibelLæseplanerVideoer
Download appen
Sprogvælger
Søgeikon

Populære bibelvers fra GENESIS 7

1

GENESIS 7:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.

Sammenlign

Udforsk GENESIS 7:1

2

GENESIS 7:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Sammenlign

Udforsk GENESIS 7:24

3

GENESIS 7:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.

Sammenlign

Udforsk GENESIS 7:11

4

GENESIS 7:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali pa dziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa pa dziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.

Sammenlign

Udforsk GENESIS 7:23

5

GENESIS 7:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo mvula inali pa dziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.

Sammenlign

Udforsk GENESIS 7:12

Forrige Kapitel
Næste Kapitel
YouVersion

Opmuntrer og udfordrer dig til at søge intimitet med Gud hver dag.

Tjeneste

Om

Karrierer

Bliv frivillig

Blog

Presse

Nyttige links

Hjælp

Donér

Bibeloversættelser

Lydbibler

Bibelsprog

Dagens vers


Et digitalt ministerium af

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

PrivatlivspolitikBetingelser
Procedure for offentliggørelse af sikkerhedssårbarheder
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Hjem

Bibel

Læseplaner

Videoer