I-Logo ye-YouVersion
IBhayibheliAmapulaniAmavidiyo
Thola i App
Okukhetha Ulimi
Isici soku Sesha

Amavesi eBhayibheli adumile avela kokuthi YOHANE 17

1

YOHANE 17:17

Buku Lopatulika

BLP-2018

Patulani iwo m'choonadi; mau anu ndi choonadi.

Qhathanisa

Hlola YOHANE 17:17

2

YOHANE 17:3

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma moyo wosatha ndi uwu, kuti akadziwe Inu Mulungu woona yekha, ndi Yesu Khristu amene munamtuma.

Qhathanisa

Hlola YOHANE 17:3

3

YOHANE 17:20-21

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma sindipempherera iwo okha, komanso iwo akukhulupirira Ine chifukwa cha mau ao; kuti onse akakhale amodzi, monga Inu Atate mwa Ine, ndi Ine mwa Inu, kuti iwonso akakhale mwa Ife: kuti dziko lapansi likakhulupirire kuti Inu munandituma Ine.

Qhathanisa

Hlola YOHANE 17:20-21

4

YOHANE 17:15

Buku Lopatulika

BLP-2018

Sindipempha kuti muwachotse iwo m'dziko lapansi, koma kuti muwasunge iwo kuletsa woipayo.

Qhathanisa

Hlola YOHANE 17:15

5

YOHANE 17:22-23

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo ulemerero umene mwandipatsa Ine ndapatsa iwo; kuti akhale amodzi, monga Ife tili mmodzi; Ine mwa iwo, ndi Inu mwa Ine, kuti akhale angwiro mwa mmodzi; kuti dziko lapansi lizindikire kuti Inu munandituma Ine, nimunawakonda iwo, monga momwe munakonda Ine.

Qhathanisa

Hlola YOHANE 17:22-23

Uhlelo Lwamahhala Lokufunda nokuthandaza okuhlobene ne YOHANE 17

Isahluko esedlule
Isahluko esilandelayo
I-YouVersion'

Ukukukhuthaza nokukubekela inselelo yokufuna ubudlelwano noNkulunkulu nsuku zonke.

Inkonzo

Mayelana

Imisebenzi

Volontiya

I-Blogi

Abezindaba

Izixhumanisi Eziwusizo

Usizo

Nikela

Izinguqulo zeBhayibheli

AmaBhayibheli Alalelwayo

Izilwimi zeBhayibheli

Ivesi losuku


Inkonzo yedijithali ye

Life.Church
English (US)

©2025 I-Life.Church / YouVersion

Inqubomgomo yobumfihloImibandela
Uhlelo Lokudalula Ubungozi
U-FacebookU-TwitterI-InstagramI-YouTubeI-Pinterest

Ikhaya

IBhayibheli

Amapulani

Amavidiyo