YouVersion Logo
بائبلمطالعاتی منصوبہVideos
اپلی کیشن حاصل کریں
زبان کا انتخاب کنندہ
تلاش

Genesis 7 سے مشہور بائبلی آیات

1

Genesis 7:1

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Yehova anati kwa Nowa, “Lowa mu chombo iwe ndi banja lako lonse, chifukwa ndaona kuti ndiwe wolungama mu mʼbado uwu.

موازنہ

تلاش Genesis 7:1

2

Genesis 7:24

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Madziwo anadzaza dziko lonse lapansi kwa masiku 150.

موازنہ

تلاش Genesis 7:24

3

Genesis 7:11

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pa tsiku la 17 la mwezi wachiwiri, Nowa ali ndi zaka 600, akasupe onse akuya kwambiri anasefuka ndiponso zitseko za madzi akumwamba zinatsekuka.

موازنہ

تلاش Genesis 7:11

4

Genesis 7:23

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Chamoyo chilichonse pa dziko lapansi chinawonongedwa, kuyambira munthu, nyama, zokwawa ndi mbalame. Nowa yekha ndiye anatsala pamodzi ndi onse amene anali naye.

موازنہ

تلاش Genesis 7:23

5

Genesis 7:12

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo mvula inagwa pa dziko lapansi masiku makumi anayi usana ndi usiku.

موازنہ

تلاش Genesis 7:12

پچھلا باب
اگلا باب
YouVersion

آپ کو ہر روز خدا کے ساتھ قربت حاصل کرنے کی ترغیب دینا اور چیلنج کرنا۔.

خدمت

بارے میں

آسامیاں

رضاکار

Blog

Press

Useful Links

مدد

ہدیہ دیں

بائبل ورژن

Audio Bibles

بائبل کی زبانیں

آج کی آیت


کی ایک ڈیجیٹل خدمت

Life.Church
اردو

©2026 Life.Church / YouVersion

Privacy Policyشرائط
حساس کا انکشاف کرنے والا عمل
FacebookTwitterInstagramیوٹیوبپنٹیرسٹ