YouVersion Logo
بائبلمطالعاتی منصوبہVideos
اپلی کیشن حاصل کریں
زبان کا انتخاب کنندہ
تلاش

Genesis 19 سے مشہور بائبلی آیات

1

Genesis 19:26

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Koma mkazi wa Loti anachewuka ndipo anasanduka mwala wa mchere.

موازنہ

تلاش Genesis 19:26

2

Genesis 19:16

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Koma Loti ankakayikabe. Koma Yehova anawachitira chifundo motero kuti anthu aja anagwira mkazi wake ndi ana ake aakazi aja nawatsogolera bwinobwino kuwatulutsa mu mzindawo.

موازنہ

تلاش Genesis 19:16

3

Genesis 19:17

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Atangowatulutsa, mmodzi wa angelowo anati, “Thawani kuti mudzipulumutse, musachewuke, musayime pena paliponse mʼchigwamo! Thawirani ku mapiri kuopa kuti mungawonongeke!”

موازنہ

تلاش Genesis 19:17

4

Genesis 19:29

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Choncho Mulungu anawononga mizinda ya ku chigwa, koma anakumbukira pemphero la Abrahamu natulutsa Loti ku sulufule ndi moto zimene zinawononga mizinda ya kumene Loti amakhalako.

موازنہ

تلاش Genesis 19:29

پچھلا باب
اگلا باب
YouVersion

آپ کو ہر روز خدا کے ساتھ قربت حاصل کرنے کی ترغیب دینا اور چیلنج کرنا۔.

خدمت

بارے میں

آسامیاں

رضاکار

Blog

Press

Useful Links

مدد

ہدیہ دیں

بائبل ورژن

Audio Bibles

بائبل کی زبانیں

آج کی آیت


کی ایک ڈیجیٹل خدمت

Life.Church
اردو

©2026 Life.Church / YouVersion

Privacy Policyشرائط
حساس کا انکشاف کرنے والا عمل
FacebookTwitterInstagramیوٹیوبپنٹیرسٹ