YouVersion Logo
بائبلمطالعاتی منصوبہVideos
اپلی کیشن حاصل کریں
زبان کا انتخاب کنندہ
تلاش

Eksodo 14 سے مشہور بائبلی آیات

1

Eksodo 14:14

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yehova adzakumenyerani nkhondo. Inu mungokhala chete.”

موازنہ

تلاش Eksodo 14:14

2

Eksodo 14:13

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Mose anayankha anthu kuti, “Musachite mantha. Imani, ndipo muone chipulumutso chimene Yehova akuchitireni lero. Aigupto amene mukuwaona lerowa simudzawaonanso.

موازنہ

تلاش Eksodo 14:13

3

Eksodo 14:16

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Nyamula ndodo yako ndi kutambasula dzanja lako kuloza ku nyanja, kugawa madzi kuti Aisraeli awoloke powuma.

موازنہ

تلاش Eksodo 14:16

4

Eksodo 14:31

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Choncho Aisraeli anaona dzanja lamphamvu la Yehova limene linagonjetsa Aigupto aja, ndipo iwo anaopa Yehova ndi kumukhulupirira pamodzi ndi mtumiki wake Mose.

موازنہ

تلاش Eksodo 14:31

پچھلا باب
اگلا باب
YouVersion

آپ کو ہر روز خدا کے ساتھ قربت حاصل کرنے کی ترغیب دینا اور چیلنج کرنا۔.

خدمت

بارے میں

آسامیاں

رضاکار

Blog

Press

Useful Links

مدد

ہدیہ دیں

بائبل ورژن

Audio Bibles

بائبل کی زبانیں

آج کی آیت


کی ایک ڈیجیٹل خدمت

Life.Church
اردو

©2026 Life.Church / YouVersion

Privacy Policyشرائط
حساس کا انکشاف کرنے والا عمل
FacebookTwitterInstagramیوٹیوبپنٹیرسٹ