YouVersion Logo
Китоби МуқаддасНақшаҳоВидео
Get the app
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from Lk. 20

1

Lk. 20:25

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Iwo aja adati, “Zonse ndi za Mfumu ya ku Roma.” Apo Yesu adaŵauza kuti, “Tsono perekani kwa Mfumu zake za Mfumu, ndiponso kwa Mulungu zake za Mulungu.”

Муқоиса

Explore Lk. 20:25

2

Lk. 20:17

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Koma Yesu adaŵayang'ana nati, “Nanga tsono tanthauzo lake nchiyani Malembo aŵa akuti, “ ‘Mwala umene amisiri omanga nyumba adaaukana, womwewo wasanduka mwala wapangodya, wofunika koposa?’

Муқоиса

Explore Lk. 20:17

3

Lk. 20:46-47

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

“Chenjera nawoni aphunzitsi a Malamulo. Amakonda kuyenda atavala mikanjo yaitali, ndi kuti anthu aziŵalonjera mwaulemu pa misika. Amakonda mipando yaulemu kwambiri m'nyumba zamapemphero ndiponso malo olemekezeka pa maphwando. Koma amaŵadyera chuma chao azimai amasiye, nkumapemphera mapemphero ataliatali monyengezera. Anthu ameneŵa adzalangidwa koposa.”

Муқоиса

Explore Lk. 20:46-47

Нақшаҳои хониши ройгон ва садоқатҳои марбут ба Lk. 20

Боби гузашта
Боби навбати
YouVersion

Encouraging and challenging you to seek intimacy with God every day.

Ministry

Дар бораи

Careers

Ихтиёрӣ

Блог

Пахш кунед

Useful Links

Кӯмак

Хайрия кардан

Bible Versions

Audio Bibles

Забонҳои Китоби Муқаддас

Ояти Рӯз


A Digital Ministry of

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Сиёсати МахфӣШартҳо
Vulnerability Disclosure Program
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Асосӣ

Китоби Муқаддас

Нақшаҳо

Видео