YouVersion Logo
Китоби МуқаддасНақшаҳоВидео
Get the app
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from Luka 24

1

Luka 24:49

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ine ndidzakutumizirani chimene Atate anga analonjeza. Koma khalani mu mzinda muno mpaka mutavekedwa mphamvu yochokera kumwamba.”

Муқоиса

Explore Luka 24:49

2

Luka 24:6

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Iye sali muno ayi. Wauka! Kumbukirani zimene anakuwuzani pamene anali nanu ku Galileya

Муқоиса

Explore Luka 24:6

3

Luka 24:31-32

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Kenaka maso awo anatsekuka ndipo anamuzindikira Iye, ndipo anachoka pakati pawo. Iwo anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Kodi mitima yathu sinali kutentha mʼkati mwathu pamene Iye ankayankhulana nafe pa njira ndi mmene anatitsekulira malemba?”

Муқоиса

Explore Luka 24:31-32

4

Luka 24:46-47

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Iye anawawuza kuti, “Izi ndi zimene zinalembedwa: Khristu adzazunzika ndipo adzauka kwa akufa tsiku lachitatu. Ndipo kutembenuka mtima ndi kukhululukidwa kwa machimo zidzalalikidwa mu dzina lake kwa anthu amitundu yonse kuyambira mu Yerusalemu.

Муқоиса

Explore Luka 24:46-47

5

Luka 24:2-3

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Anaona mwala wa pa manda utagubuduzika ndipo atalowamo sanapeze mtembo wa Ambuye Yesu.

Муқоиса

Explore Luka 24:2-3

Нақшаҳои хониши ройгон ва садоқатҳои марбут ба Luka 24

Боби гузашта
Боби навбати
YouVersion

Encouraging and challenging you to seek intimacy with God every day.

Ministry

Дар бораи

Careers

Ихтиёрӣ

Блог

Пахш кунед

Useful Links

Кӯмак

Хайрия кардан

Bible Versions

Audio Bibles

Забонҳои Китоби Муқаддас

Ояти Рӯз


A Digital Ministry of

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Сиёсати МахфӣШартҳо
Vulnerability Disclosure Program
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Асосӣ

Китоби Муқаддас

Нақшаҳо

Видео