Mufananidzo weYouVersion
Mucherechedzo Wekutsvaka

Zefaniya 2:11

Zefaniya 2:11 CCL

Yehova adzawachititsa mantha kwambiri pamene adzawononga milungu yonse ya mʼdzikomo. Ndipo mitundu ya anthu pa dziko lonse idzamulambira, uliwonse ku dziko la kwawo.