Mufananidzo weYouVersion
Mucherechedzo Wekutsvaka

Zefaniya 1:14

Zefaniya 1:14 CCL

Tsiku lalikulu la Yehova layandikira, layandikira ndipo lifika msanga. Tamverani! Kulira kwa pa tsiku la Yehova kudzakhala kowawa, ngakhale munthu wolimba mtima adzalira kwambiri.