Mufananidzo weYouVersion
Mucherechedzo Wekutsvaka

Zekariya 8:13

Zekariya 8:13 CCL

Monga mwakhala muli chinthu chotembereredwa pakati pa mitundu ina ya anthu, inu Yuda ndi Israeli, choncho ndidzakupulumutsani, ndipo mudzakhala dalitso. Musachite mantha, koma limbani mtima.”