Mufananidzo weYouVersion
Mucherechedzo Wekutsvaka

Marko 9:42

Marko 9:42 CCL

“Ndipo ngati wina aliyense achimwitsa mmodzi wa ana angʼono awa amene akhulupirira Ine, kukanakhala bwino kwa iye kuti aponyedwe mʼnyanja atamangiriridwa mwala waukulu mʼkhosi mwake.