Mufananidzo weYouVersion
Mucherechedzo Wekutsvaka

Marko 4:26-27

Marko 4:26-27 CCL

Iye anatinso, “Umu ndi mmene ulili ufumu wa Mulungu. Munthu amafesa mbewu mʼnthaka. Usiku ndi usana, kaya agona kapena adzuka, mbewu imamera ndi kukula, ngakhale sadziwa mmene zimachitikira.