Mufananidzo weYouVersion
Mucherechedzo Wekutsvaka

Marko 13:11

Marko 13:11 CCL

Nthawi iliyonse pamene mwamangidwa ndi kuyimbidwa mlandu, musadandaule za zimene mudzanena. Zimene mudzapatsidwe pa nthawiyo yankhulani; pakuti sindinu amene mudzayankhula, koma Mzimu Woyera.