Mufananidzo weYouVersion
Mucherechedzo Wekutsvaka

Malaki 2:16

Malaki 2:16 CCL

Yehova Mulungu wa Israeli akuti, “Ndimadana ndi kulekana ukwati. Ndimadana ndi munthu wochita zankhanza zotere kwa mkazi wake,” akutero Yehova Wamphamvuzonse. Choncho tetezani mzimu wanu, ndipo musakhale osakhulupirika.