1
Zekariya 7:9
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
“Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Muziweruza molungama; muzichitirana chifundo ndi kumverana chisoni.
Yenzanisa
Ongorora {{vhesi}}
2
Zekariya 7:10
Musamazunze akazi amasiye kapena ana amasiye, alendo kapena osauka. Musamaganizirane zoyipa mʼmitima mwanu.’