1
Yoh. 20:21-22
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Yesu adatinso, “Mtendere ukhale nanu. Monga Atate adandituma, Inenso ndikukutumani.” Pambuyo pake adaŵauzira mpweya nati, “Landirani Mzimu Woyera.
සසඳන්න
Yoh. 20:21-22 ගවේෂණය කරන්න
2
Yoh. 20:29
Yesu adati, “Kodi wakhulupirira chifukwa wandiwona? Ngwodala amene amakhulupirira ngakhale sadaone.”
Yoh. 20:29 ගවේෂණය කරන්න
3
Yoh. 20:27-28
Atatero, adauza Tomasi kuti, “Ika chala chako apa, ona manja anga. Tambalitsa dzanja lako, ulipise m'nthiti mwangamu. Leka kukayika, uyambepo kukhulupirira.” Tomasi adati, “Ambuye anga! Mulungu wanga!”
Yoh. 20:27-28 ගවේෂණය කරන්න
නිවස
බයිබලය
සැලසුම්
වීඩියෝ