1
Luka 19:10
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Pajatu Mwana wa Munthu anabwera kudzafunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.”
සසඳන්න
Luka 19:10 ගවේෂණය කරන්න
2
Luka 19:38
“Yodala mfumu imene ikubwera mʼdzina la Ambuye!” “Mtendere kumwamba ndi ulemerero mmwambamwamba!”
Luka 19:38 ගවේෂණය කරන්න
3
Luka 19:9
Yesu anati kwa iye, “Lero chipulumutso chafika mʼnyumba ino, chifukwa munthu uyu nayenso ndi mwana wa Abrahamu.
Luka 19:9 ගවේෂණය කරන්න
4
Luka 19:5-6
Yesu atafika pa malopo, anayangʼana mmwamba ndipo anati kwa iye, “Zakeyu, tsika msangamsanga. Ine ndiyenera kukhala mʼnyumba mwako lero.” Ndipo nthawi yomweyo anatsika ndipo anamulandira mosangalala.
Luka 19:5-6 ගවේෂණය කරන්න
5
Luka 19:8
Koma Zakeyu anayimirira ndipo anati kwa Ambuye, “Taonani Ambuye! Theka la chuma changa ndipereka kwa osauka ndipo ngati ndinamubera wina aliyense pa chilichonse, ndidzamubwezera mochulukitsa kanayi.”
Luka 19:8 ගවේෂණය කරන්න
6
Luka 19:39-40
Ena mwa Afarisi mʼgulumo anati kwa Yesu, “Aphunzitsi, adzudzuleni ophunzira anu!” Iye anayankha kuti, “Ine ndikukuwuzani kuti, ngati atakhala chete, miyala idzafuwula.”
Luka 19:39-40 ගවේෂණය කරන්න
නිවස
බයිබලය
සැලසුම්
වීඩියෝ