1
Gen. 16:13
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Tsono Hagara adatcha Chauta amene adalankhula naye kuti, “Inu ndinu Mulungu wondipenya,” poti adati, “Pano ndamuwona Iye amene amandipenya.”
Compare
Gen. 16:13ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
2
Gen. 16:11
Popitiriza mau mngeloyo adati, “Tsopano uli pafupi kukhala ndi mwana wamwamuna, udzamutche Ismaele, ndiye kuti Chauta wamva kulira kwako pa zovuta zako.
Gen. 16:11ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
3
Gen. 16:12
Koma mwana wako adzakhala ndi mtima wa chilombo, adzadana ndi aliyense, ndipo anthu onse adzadana naye. Adzakhala akudana ndi abale ake onse.”
Gen. 16:12ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
Home
ਬਾਈਬਲ
Plans
ਵੀਡੀਓ