1
EKSODO 22:22-23
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Musazunza mkazi wamasiye, kapena mwana wamasiye aliyense. Ukawazunza ndi kakuti konse, nakandilirira pang'ono ponse iwowa, ndidzamvadi kulira kwao
Compare
EKSODO 22:22-23ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
2
EKSODO 22:21
Ndipo usasautsa mlendo kapena kumpsinja; pakuti munali alendo m'dziko la Ejipito.
EKSODO 22:21ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
3
EKSODO 22:18
Wanyanga usamlola akhale ndi moyo.
EKSODO 22:18ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
4
EKSODO 22:25
Ukakongoletsa ndalama anthu anga osauka okhala nanu, usamkhalira ngati wangongole; usamwerengera phindu.
EKSODO 22:25ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
Home
ਬਾਈਬਲ
Plans
ਵੀਡੀਓ