EKSODO 13:21-22
EKSODO 13:21-22 BLPB2014
Ndipo Yehova anawatsogolera usana ndi mtambo njo kuwatsogolera m'njira; ndi usiku ndi moto njo, wakuwawalitsira; kuti ayende usana ndi usiku; sanachotse mtambo usana, kapena mtambo wamoto usiku, pamaso pa anthu.


