1
MARKO 11:24
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Chifukwa chake ndinena ndi inu, Zinthu zilizonse mukazipemphera ndi kuzipempha, khulupirirani kuti mwazilandira, ndipo mudzakhala nazo.
ႏွိုင္းယွဥ္
MARKO 11:24ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
MARKO 11:23
Ndithu ndinena ndi inu, kuti, Munthu aliyense akanena ndi phiri ili, Tanyamulidwa, nuponyedwe m'nyanja; wosakayika mumtima mwake, koma adzakhulupirira kuti chimene achinena chichitidwa, adzakhala nacho.
MARKO 11:23ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
3
MARKO 11:25
Ndipo pamene muimirira ndi kupemphera, khululukirani, ngati munthu wakulakwirani kanthu; kuti Atate wanunso ali Kumwamba akhululukire inu zolakwa zanu.
MARKO 11:25ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
4
MARKO 11:22
Ndipo Yesu anayankha nanena nao, Khulupirirani Mulungu.
MARKO 11:22ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
5
MARKO 11:17
Ndipo anaphunzitsa, nanena nao, Sichilembedwa kodi, Nyumba yanga idzatchedwa nyumba yakupempheramo anthu a mitundu yonse? Koma inu mwaiyesa phanga la achifwamba.
MARKO 11:17ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
6
MARKO 11:9
Ndipo akutsogolera, ndi iwo akutsata, anafuula, Hosana; Wolemekezeka Iye wakudza m'dzina la Ambuye
MARKO 11:9ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
7
MARKO 11:10
Wolemekezeka Ufumu ulinkudza, wa atate wathu Davide; Hosana m'Kumwambamwamba.
MARKO 11:10ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား