1
GENESIS 41:16
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo Yosefe anayankha Farao kuti, Si mwa ine; koma Mulungu adzayankha Farao mwamtendere.
ႏွိုင္းယွဥ္
GENESIS 41:16ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
GENESIS 41:38
Ndipo Farao anati kwa anyamata ake, Kodi ife tidzaone munthu ngati uyu, mzimu wa Mulungu uli m'mtima mwake?
GENESIS 41:38ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
3
GENESIS 41:39-40
Ndipo Farao anati kwa Yosefe, Popeza Mulungu wakuonetsa iwe zonsezo palibe wina wakuzindikira ndi wanzeru ngati iwe. Uziyang'anira pa nyumba yanga, ndipo anthu anga onse adzalamulidwa mwa mau ako; pa mpando wachifumu pokha ine ndidzakuposa iwe.
GENESIS 41:39-40ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
4
GENESIS 41:52
Ndipo dzina la wachiwiri anamutcha Efuremu: chifukwa Mulungu anandibalitsa ine m'dziko la kusauka kwanga.
GENESIS 41:52ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
5
GENESIS 41:51
Ndipo Yosefe anamutcha dzina la woyamba Manase, chifukwa anati iye, Mulungu wandiiwalitsa ine zovuta zanga zonse, ndi nyumba yonse ya atate wanga.
GENESIS 41:51ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား