1
EKSODO 8:18-19
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Alembi anateronso ndi matsenga ao kuonetsa nsabwe, koma sanakhoza; ndipo panali nsabwe pa anthu, ndi pa zoweta. Pamenepo alembi anati kwa Farao, Chala cha Mulungu ichi; koma mtima wa Farao unalimba, osamvera iwo; monga adalankhula Yehova.
ႏွိုင္းယွဥ္
EKSODO 8:18-19ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
EKSODO 8:1
Ndipo Yehova anati kwa Mose, Lowa kwa Farao, nunene naye, Atero Yehova, Lola anthu anga amuke, kuti anditumikire.
EKSODO 8:1ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
3
EKSODO 8:15
Koma pamene Farao anaona kuti panali kupuma, anaumitsa mtima wake, osamvera iwo; monga adalankhula Yehova.
EKSODO 8:15ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
4
EKSODO 8:2
Ndipo ukakana kuwalola amuke, taona, Ine ndidzapanda dziko lako lonse ndi achule
EKSODO 8:2ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
5
EKSODO 8:16
Ndipo Yehova anati kwa Mose, Nena ndi Aroni, Samula ndodo yako, nupande fumbi lapansi, kuti lisanduke nsabwe m'dziko lonse la Ejipito.
EKSODO 8:16ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
6
EKSODO 8:24
Ndipo Yehova anachita chomwecho; ndipo kunafika magulu a mizaza m'nyumba ya Farao, ndi m'nyumba za anyamata ake, ndi m'dziko lonse la Ejipito; dziko linaipatu chifukwa cha mizazayo.
EKSODO 8:24ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား