1
EKSODO 29:45-46
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo ndidzakhala pakati pa ana a Israele, ndi kukhala Mulungu wao. Ndipo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wao, amene ndinawatulutsa m'dziko la Ejipito, kuti ndikhale pakati pao. Ine ndine Yehova Mulungu wao.
ႏွိုင္းယွဥ္
EKSODO 29:45-46ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား