1
EKSODO 22:22-23
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Musazunza mkazi wamasiye, kapena mwana wamasiye aliyense. Ukawazunza ndi kakuti konse, nakandilirira pang'ono ponse iwowa, ndidzamvadi kulira kwao
ႏွိုင္းယွဥ္
EKSODO 22:22-23ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
EKSODO 22:21
Ndipo usasautsa mlendo kapena kumpsinja; pakuti munali alendo m'dziko la Ejipito.
EKSODO 22:21ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
3
EKSODO 22:18
Wanyanga usamlola akhale ndi moyo.
EKSODO 22:18ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
4
EKSODO 22:25
Ukakongoletsa ndalama anthu anga osauka okhala nanu, usamkhalira ngati wangongole; usamwerengera phindu.
EKSODO 22:25ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား