1
EKSODO 14:14
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Yehova adzakugwirirani nkhondo, ndipo inu mudzakhala chete.
ႏွိုင္းယွဥ္
EKSODO 14:14ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
EKSODO 14:13
Ndipo Mose ananena ndi anthu, Musaope, chilimikani, ndipo penyani chipulumutso cha Yehova, chimene adzakuchitirani lero; pakuti Aejipito mwawaona lerowa, simudzawaonanso konse.
EKSODO 14:13ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
3
EKSODO 14:16
Ndipo iwe nyamula ndodo yako, nutambasulire dzanja lako kunyanja, nuigawe, kuti ana a Israele alowe pakati pa nyanja pouma.
EKSODO 14:16ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
4
EKSODO 14:31
Ndipo Israele anaiona ntchito yaikulu imene Yehova anachitira Aejipito, ndipo anthuwo anaopa Yehova; nakhulupirira Yehova ndi mtumiki wake Mose.
EKSODO 14:31ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား