1
EKSODO 1:17
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Koma anamwino anaopa Mulungu, ndipo sanachite monga mfumu ya Aejipito inawauza, koma analeka ana amuna akhale ndi moyo.
ႏွိုင္းယွဥ္
EKSODO 1:17ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
EKSODO 1:12
Koma monga momwe anawasautsiramo, momwemo anachuluka, momwemonso anafalikira. Ndipo anavutika chifukwa cha ana Israele.
EKSODO 1:12ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
3
EKSODO 1:21
Ndipo kunatero kuti, popeza anamwino anaopa Mulungu, Iye anawamangitsira mabanja.
EKSODO 1:21ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
4
EKSODO 1:8
Pamenepo inalowa mfumu yatsopano m'ufumu wa Ejipito, imene siinadziwa Yosefe.
EKSODO 1:8ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား