1
Matayo 26:41
Nyanja
NTNYBL2025
Chezelani ni kupembhela kuti msadalowa mu mayeselo. Mtima ufuna kuchita yayo yafunika, nambho thupi lilibe mbhavu.”
താരതമ്യം
Matayo 26:41 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
Matayo 26:38
Kumeneko wadaakambila, “Nili ni chisoni chachikulu mumtima mwanga icho chikhoza kunipha. Khalani pano ni muchezele pamojhi ni ine.”
Matayo 26:38 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
Matayo 26:39
Wadapita pachogolo pang'ono, wadagwa panjhi chifufumimba ni kupembhela, “Atate wanga, ngati ikhozeka, nichocheleni chikho ichi cha mavuto! Chipano osati ngati umo nifunila ine, nambho ngati umo mufunila imwe.”
Matayo 26:39 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
Matayo 26:28
uwu nde mwazi wanga uwo uchimikiza chipangano, umwazika ndande ya ambili dala machimo yao yalekeleledwe.
Matayo 26:28 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
Matayo 26:26
Yapo amadya Yesu wadatenga bumunda, wadayamika, wadaubandhula, ni kwapacha oyaluzidwa wake nikukamba, “Tengani mudye, ili nithupi langa.”
Matayo 26:26 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
Matayo 26:27
Ndiipo wadatenga chikho, wadayamika Mnungu, ni kwaapacha oyaluzidwa wake niwakamba, “Mwaonjhe mchimwele chikho ichi
Matayo 26:27 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
7
Matayo 26:40
Ndiipo wadabwela kwa oyaluzidwa wake ni kwaapheza agona, wadamkambila Petulo, “Ikhala bwanji simdakhoze kuchezelela ni ine ata kwa saa imojhipe?
Matayo 26:40 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
8
Matayo 26:29
Nikukambilani, sinimwanjho divai iyi mbaka siku ilo sinimwe divai yachipano ni anyiimwe mu Ufumu wa Atate wanga.”
Matayo 26:29 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
9
Matayo 26:75
Ndiipo Petulo wadakumbukila mau yajha wadakamba Yesu, “Tambala wakali osalile, siunikane katatu.” Wadapita kubwalo, wadalila kwa kubuula.
Matayo 26:75 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
10
Matayo 26:46
Imani tijhipita. Yujha waning'anamuka watokujha.”
Matayo 26:46 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
11
Matayo 26:52
Ndiipo Yesu wadamkambila, “Bwezela upanga wako mmalo mwake, pakuti waliyonjhe wakupha kwa upanga, siwaphedwe kwa upanga.
Matayo 26:52 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ