1
Matayo 18:20
Nyanja
NTNYBL2025
Pakuti yapo asonghana wandhu awili kapina atatu kwa jhina langa, ine nili pamojhi nao.”
താരതമ്യം
Matayo 18:20 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
Matayo 18:19
“Zene nikukambilani, awili pakati panu akavomelezana pajhiko la panjhi kuusu chilichonjhe icho afuna kupembha, Atate wanga a kumwamba siakuchitileni.
Matayo 18:19 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
Matayo 18:2-3
Yesu wadamtana mwana wamng'ono ni kumwimika pakati pao, Ndiipo wadaakambila, “Zene nikukambilani, ngati simng'anamuka ni kulingana ni wana waang'onoang'ono, simulowa mu Ufumu wa kumwamba.
Matayo 18:2-3 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
Matayo 18:4
Waliyonjhe uyo wajhichepecha ngati mwana uyu, nde uyo siwakhale wamkulu mu Ufumu wa kumwamba.
Matayo 18:4 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
Matayo 18:5
Uyo wamlandila mwana wamng'ono ngati uyu kwa jhina langa, wanilandila ine.”
Matayo 18:5 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
Matayo 18:18
“Zene ikukambilani, yayo simuyamange pajhiko la panjhi chinchijha siyamangidwe kumwamba, ni icho simuchimasule pajhiko la panjhi chinchijha sichimasulidwe kumwamba.
Matayo 18:18 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
7
Matayo 18:35
Yesu wadamaliza pokamba, “Umu ndeumo Atate wanga akumwamba siakuchiteni ngati simwaalekelela achanjanu volakwa vao.”
Matayo 18:35 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
8
Matayo 18:6
“Ngati mundhu waliyonjhe uyo wamchiticha mmojhi wa wana yawa kuchita chimo, idakakhala mbasa kwa mundhu mmeneyo wamangidwe mbhelo mkhosi mwake ni kubizidwa kuchilundu.
Matayo 18:6 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
9
Matayo 18:12
“Muona bwanji ngati mundhu wali ni mbelele miya mojha, ikasowa imojhi, wachita bwanji? Wazisia zijha tisini ni tisa mkhola, nikupita kuifunafuna ijha yasowa.
Matayo 18:12 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ