1
Matayo 16:24
Nyanja
NTNYBL2025
Ndiipo Yesu wadaakambila oyaluzidwa wake, “Mundhu uyo wafuna kunichata, poyamba wafunika wajhikane mwenewake ni kuutenga mtanda wake, wanichate.
താരതമ്യം
Matayo 16:24 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
Matayo 16:18
Niine nikukambila iwe Petulo, iwe ni mwala waukulu, ni pamwamba pa mwala umenewo, siniumange mpingo wanga, ni mbhavu za kumdima sizikhoza kulimbana nawo.
Matayo 16:18 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
Matayo 16:19
Nikupacha ufunguo wa ufumu wa kumwamba ni chilichonjhe icho siuchimange pajhiko, sichimangidwe kumwamba, chilichonjhe icho siuchimasule pajhiko, sichimasulidwenjho kumwamba.”
Matayo 16:19 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
Matayo 16:25
Pakuti, mundhu uyo wafuna kuulamicha umoyo wake, siwautaize, ni mundhu uyo siwautaize umoyo wake ndande ya ine, siwaupate.
Matayo 16:25 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
Matayo 16:26
Pakuti, mundhu siwapate phindu lanji wakayapata yonjhe yali pajhiko, nambho wautaize umoyo wake? Kapina mundhu siwachoche chiyani kuti waupate umoyo wake?
Matayo 16:26 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
Matayo 16:15-16
Yesu wadaafunjha, “Bwanji, ni anyiimwe mkamba kuti ine ni yani?” Simoni uyo watanidwa Petulo wadayangha, “Iwe nde Kilisito muomboli, Mwana wa Mnungu wali wamoyo.”
Matayo 16:15-16 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
7
Matayo 16:17
Yesu wadayangha, “Wapachidwa mwawi iwe Simoni mwana wa Yona, pakuti ichi wachikamba siudavunukulilidwe ni mundhu, nambho Atate wanga a kumwamba.
Matayo 16:17 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ