1
ZEKARIYA 4:6
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Pamenepo anayankha, nanena kwa ine, ndi kuti, Awa ndi mau a Yehova kwa Zerubabele, Ndi khamu la nkhondo ai, ndi mphamvu ai, koma ndi Mzimu wanga, ati Yehova wa makamu.
താരതമ്യം
ZEKARIYA 4:6 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
ZEKARIYA 4:10
Pakuti wapeputsa tsiku la tinthu tating'ono ndani? Pakuti adzakondwera, asanu ndi awiri awa, nadzaona chingwe cholungamitsira chilili m'dzanja la Zerubabele, ndiwo maso a Yehova; ayendayenda mwa dziko lonse.
ZEKARIYA 4:10 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
ZEKARIYA 4:9
Manja a Zerubabele anaika maziko a nyumba iyi, manja ake omwe adzaitsiriza; ndipo udzadziwa kuti Yehova wa makamu anandituma kwa inu.
ZEKARIYA 4:9 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ