1
MARKO 11:24
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Chifukwa chake ndinena ndi inu, Zinthu zilizonse mukazipemphera ndi kuzipempha, khulupirirani kuti mwazilandira, ndipo mudzakhala nazo.
താരതമ്യം
MARKO 11:24 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MARKO 11:23
Ndithu ndinena ndi inu, kuti, Munthu aliyense akanena ndi phiri ili, Tanyamulidwa, nuponyedwe m'nyanja; wosakayika mumtima mwake, koma adzakhulupirira kuti chimene achinena chichitidwa, adzakhala nacho.
MARKO 11:23 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MARKO 11:25
Ndipo pamene muimirira ndi kupemphera, khululukirani, ngati munthu wakulakwirani kanthu; kuti Atate wanunso ali Kumwamba akhululukire inu zolakwa zanu.
MARKO 11:25 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MARKO 11:22
Ndipo Yesu anayankha nanena nao, Khulupirirani Mulungu.
MARKO 11:22 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MARKO 11:17
Ndipo anaphunzitsa, nanena nao, Sichilembedwa kodi, Nyumba yanga idzatchedwa nyumba yakupempheramo anthu a mitundu yonse? Koma inu mwaiyesa phanga la achifwamba.
MARKO 11:17 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
MARKO 11:9
Ndipo akutsogolera, ndi iwo akutsata, anafuula, Hosana; Wolemekezeka Iye wakudza m'dzina la Ambuye
MARKO 11:9 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
7
MARKO 11:10
Wolemekezeka Ufumu ulinkudza, wa atate wathu Davide; Hosana m'Kumwambamwamba.
MARKO 11:10 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ