1
MATEYU 25:40
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo Mfumuyo idzayankha nidzati kwa iwo, Indetu ndinena kwa inu, Chifukwa munachitira ichi mmodzi wa abale anga, ngakhale ang'onong'ono awa, munandichitira ichi Ine.
താരതമ്യം
MATEYU 25:40 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MATEYU 25:21
Mbuye wake anati kwa iye, Chabwino, kapolo iwe wabwino ndi wokhulupirika; unali wokhulupirika pa zinthu zazing'ono, ndidzakhazika iwe pa zinthu zambiri; lowa iwe m'chikondwerero cha mbuye wako.
MATEYU 25:21 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MATEYU 25:29
Pakuti kwa yense amene ali nazo, kudzapatsidwa, ndipo iye adzakhala nazo zochuluka: koma kwa iye amene alibe, kudzachotsedwa, chingakhale chimene anali nacho.
MATEYU 25:29 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MATEYU 25:13
Chifukwa chake dikirani, pakuti simudziwa tsiku lake, kapena nthawi yake.
MATEYU 25:13 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MATEYU 25:35
pakuti ndinali ndi njala, ndipo munandipatsa Ine kudya; ndinali ndi ludzu, ndipo munandimwetsa Ine; ndinali mlendo, ndipo munachereza Ine
MATEYU 25:35 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
MATEYU 25:23
MATEYU 25:23 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
7
MATEYU 25:36
wamaliseche Ine, ndipo munandiveka; ndinadwala, ndipo munadza kucheza ndi Ine; ndinali m'nyumba yandende, ndipo munadza kwa Ine.
MATEYU 25:36 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ