1
MATEYU 14:30-31
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Koma m'mene iye anaiona mphepo, anaopa; ndipo poyamba kumira, anafuula, nati, Ambuye, ndipulumutseni ine! Ndipo pomwepo Yesu anatansa dzanja lake, namgwira iye, nanena naye, Iwe wokhulupirira pang'ono, wakayikiranji mtima?
താരതമ്യം
MATEYU 14:30-31 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MATEYU 14:30
Koma m'mene iye anaiona mphepo, anaopa; ndipo poyamba kumira, anafuula, nati, Ambuye, ndipulumutseni ine!
MATEYU 14:30 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MATEYU 14:27
Koma pomwepo Yesu analankhula nao, nati, Limbani mtima; ndine; musaope.
MATEYU 14:27 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MATEYU 14:28-29
Ndipo Petro anamyankha Iye nati, Ambuye, ngati ndinutu, mundiuze ndidze kwa Inu pamadzi. Ndipo Iye anati, Idza. Ndipo Petro anatsika m'ngalawa, nayenda pamadzi, kufika kwa Yesu.
MATEYU 14:28-29 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MATEYU 14:33
Ndipo iwo amene anali m'ngalawamo anamgwadira, nanena, Zoonadi, ndinu Mwana wa Mulungu.
MATEYU 14:33 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
MATEYU 14:16-17
Koma Yesu anati kwa iwo, Iwo alibe chifukwa cha kumukira, apatseni ndinu adye. Koma iwo ananena kwa Iye, Ife tilibe kanthu pano koma mikate isanu, ndi nsomba ziwiri.
MATEYU 14:16-17 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
7
MATEYU 14:18-19
Ndipo Iye anati, Mudze nazo kuno kwa Ine. Ndipo Iye analamulira makamu a anthu akhale pansi paudzu; ndipo Iye anatenga mikate isanuyo ndi nsomba ziwirizo, ndipo m'mene anayang'ana kumwamba, anadalitsa, nanyema, napatsa mikateyo kwa ophunzira, ndi ophunzira kwa makamuwo.
MATEYU 14:18-19 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
8
MATEYU 14:20
Ndipo anadya onse, nakhuta; ndipo anatola makombo otsala, nadzala madengu khumi ndi iwiri.
MATEYU 14:20 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ