1
GENESIS 29:20
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo Yakobo anamtumikira zaka zisanu ndi ziwiri chifukwa cha Rakele; koma zidamuonekera iye ngati masiku owerengeka chifukwa cha chikondi chimene anamkonda iye nacho.
താരതമ്യം
GENESIS 29:20 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
GENESIS 29:31
Pamene Yehova anaona kuti anamuda Leya, anatsegula m'mimba mwake; koma Rakele anali wouma.
GENESIS 29:31 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ