1
Eksodo 5:1
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Zitachitika izi, Mose ndi Aaroni anapita kwa Farao ndipo anati, “Yehova Mulungu wa Israeli akuti, ‘Aloleni anthu anga apite, kuti akachite chikondwerero cha Ine mʼchipululu.’ ”
ತಾಳೆಮಾಡಿ
Eksodo 5:1 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
2
Eksodo 5:23
Chipitireni changa kwa Farao kukamuyankhula mʼdzina lanu, iye wakhala akuzunza anthuwa, ndipo inu simunawapulumutse konse anthu anu.”
Eksodo 5:23 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
3
Eksodo 5:22
Mose anabwerera kwa Yehova ndipo anati, “Chonde Ambuye, chifukwa chiyani mukuzunza anthu anu? Kodi munanditumira zimenezi?
Eksodo 5:22 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
4
Eksodo 5:2
Koma Farao anati, “Yehova ndani kuti ine ndimumvere ndi kulola Aisraeli kuti apite? Ine Yehova sindikumudziwa ndipo sindilola kuti Aisraeli apite.”
Eksodo 5:2 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
5
Eksodo 5:8-9
Koma musawachepetsere chiwerengero cha njerwa chomwe munawalamulira kale kuti aziwumba. Iwowa ndi aulesi. Nʼchifukwa chake akulira kuti, ‘Tiloleni tipite tikapereke nsembe kwa Mulungu wathu.’ Muwakhawulitse ndi ntchito anthu amenewa kuti azitanganidwa, asakhale ndi mpata omvera zabodza.”
Eksodo 5:8-9 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ