YouVersion ಲೋಗೋ
ಬೈಬಲ್ಯೋಜನೆಗಳುವೀಡಿಯೊಗಳು
ಆ್ಯಪ್ ನ್ನು ಪಡೆಯಿರಿ
ಭಾಷಾ ಆಯ್ಕೆದಾರ
ಹುಡುಕಾಟ ಐಕಾನ್

Eksodo 31ರಿಂದ ಜನಪ್ರಿಯ ಬೈಬಲ್ ವಚನಗಳು

1

Eksodo 31:2-5

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Taona, ndasankha Bezaleli mwana wa Uri, mwana wa Huri, wa fuko la Yuda. Ndipo ndamudzaza ndi Mzimu wa Mulungu kotero kuti ali ndi luso ndi nzeru zomvetsa zinthu ndipo akudziwa bwino ntchito zonse zamanja monga izi: Kulemba ndondomeko ya ntchito zaluso ndi kupanga zinthu zagolide, zasiliva ndi zamkuwa, kusema ndi kuyika miyala yokongola, kukonza zinthu zamatabwa ndiponso kugwira ntchito ina iliyonse yamanja.

ತಾಳೆಮಾಡಿ

Eksodo 31:2-5 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ

2

Eksodo 31:13

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Uza ana a Israeli kuti azisunga Masabata anga. Ichi chidzakhala chizindikiro pakati pa inu ndi Ine pamodzi ndi zidzukulu zanu mʼtsogolomo, chosonyeza kuti Ine ndine amene ndimakuyeretsani.

ತಾಳೆಮಾಡಿ

Eksodo 31:13 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ

3

Eksodo 31:17

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Tsiku la Sabata lidzakhala chizindikiro chamuyaya pakati pa Ine ndi Aisraeli chosonyeza kuti Yehova analenga za kumwamba ndi dziko lapansi kwa masiku asanu ndi limodzi ndi kuti pa tsiku lachisanu ndi chiwiri analeka kugwira ntchito napumula.”

ತಾಳೆಮಾಡಿ

Eksodo 31:17 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ

Eksodo 31 ಗೆ ಸಂಬಂಧಿಸಿದ ಉಚಿತ ಓದುವ ಯೋಜನೆಗಳು ಮತ್ತು ಆರಾಧನೆಗಳು

ಹಿಂದಿನ ಅಧ್ಯಾಯ
ಮುಂದಿನ ಅಧ್ಯಾಯ
YouVersion

Encouraging and challenging you to seek intimacy with God every day.

Ministry

ಬಗ್ಗೆ

Careers

ಸ್ವಯಂಸೇವಕ

ಬ್ಲಾಗ್

ಒತ್ತಿ

Useful Links

ಸಹಾಯ

ದೇಣಿಗೆ

ಬೈಬಲ್ ಆವೃತ್ತಿಗಳು

ಆಡಿಯೋ ಬೈಬಲ್‌ಗಳು

ಬೈಬಲ್ ಭಾಷೆಗಳು

ಈ ದಿನದ ವಚನ


ಡಿಜಿಟಲ್ ಸಚಿವಾಲಯ

Life.Church
English (US)

©2026 ಲೈಫ್.ಚರ್ಚ್ / ಯೂವರ್ಷನ್

ಗೌಪ್ಯತಾ ನೀತಿನಿಯಮಗಳು
ದುರ್ಬಲತೆ ಬಹಿರಂಗಪಡಿಸುವಿಕೆ ಕಾರ್ಯಕ್ರಮ
ಫೇಸ್ಬುಕ್ಟ್ವಿಟರ್ಇನ್ಸ್ ಟಾ ಗ್ರಾಮ್ಯೂಟ್ಯೂಬ್ಪಿನ್‌ಟರೆಸ್ಟ್