1
Eksodo 24:17-18
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Ulemerero wa Yehova uja unkaoneka ngati malawi a moto pamwamba pa phirilo. Ndipo Mose analowa mʼmitambo nakwera phiri. Iye anakhala ku phiriko 40 usana ndi usiku.
ತಾಳೆಮಾಡಿ
Eksodo 24:17-18 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
2
Eksodo 24:16
Ulemerero wa Yehova unakhala pa phiri la Sinai, ndipo mtambo unaphimba phirilo kwa masiku asanu ndi limodzi. Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri Yehova anayitana Mose kuchokera mu mtambowo.
Eksodo 24:16 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
3
Eksodo 24:12
Yehova anati kwa Mose, “Bwera kwa ine ku phiri kuno, ndipo udikire konkuno. Ndidzakupatsa miyala imene ndalembapo malemba kuti ndiwaphunzitse.”
Eksodo 24:12 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ