1
Eksodo 22:22-23
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
“Musazunze mkazi wamasiye kapena mwana wamasiye. Ngati muwazunza ndipo iwo nʼkulirira kwa Ine, ndidzamva kulira kwawo.
ತಾಳೆಮಾಡಿ
Eksodo 22:22-23 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
2
Eksodo 22:21
“Musazunze mlendo kapena kumuchitira nkhanza, pakuti inu munali alendo mʼdziko la Igupto.
Eksodo 22:21 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
3
Eksodo 22:18
“Musayilole mfiti yayikazi kuti ikhale ndi moyo.
Eksodo 22:18 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
4
Eksodo 22:25
“Ngati mukongoza ndalama kwa mʼbale wanu amene ndi mʼmphawi pakati panu, musadzamuchite monga zimene amachita wokongoza ndalama. Musadzamuyikire chiwongoladzanja.
Eksodo 22:25 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ